Matsiku amakedzana, anthu sanali kudziwa ciliconse. Sanadziwe kubzala mbeu, mwina kusoka zovala, mwina kupanga zitsulo zansimbi. Nyame mulungu wakumwamba anali ndi nzelu pa zonse zamdziko lapansi. Nzeluzi anazisungila bwino mu mbiya.
Longe, longe antaŭe la homoj ne sciis ion ajn. Ili ne sciis kiel farmi kultivaĵojn aŭ kiel teksi tukojn aŭ kiel fari ferajn ilojn. La dio Nyame supre en la ĉielo havis ĉiun saĝecon de la mondo. Li tenis ĝin sekura en argila kruĉo.
Tsiku lina, Nyame anaganiza kupatsa Anansi mbiya ya nzelu. Nthawi iliyonse Anansi akayangana mumbiya, anaphunzilamo cinthu cina catsopano. Cinali cokondweletsa kwambili!
Unu tagon, Nyame decidis ke li donos la kruĉon de saĝeco al Anansi. Ĉiam kiam Anansi rigardis en la argilan kruĉon, li lernis ion novan. Ĝi estis tiel ekscita!
Anansi waumbombo anaganiza, “Ndizaisunga bwino mbiya pamwamba pa mtengo wautali. Motelo izakhala yanga ndekha!” Anatenga nthambo yaitali, yakumangilila mbiya ndikuimangilila pamimba pake. Anayamba kukwela mtengo. Koma cinali cobvuta kukwela cifukwa mbiya inali kumugunda kumyendo nthawi yonse.
Avida Anansi pensis, “mi tenos la kruĉon ĉe la supro de alta arbo. Tiel mi povas havi ĉion por mi mem!” Li ŝpinis longan fadenon, bobenis ĝin ĉirkaŭ la argilan kruĉon kaj ligis ĝin al sia stomako. Li komencis grimpi la arbon. Sed estis malfacile grimpi la arbon kun la kruĉo frapanta liajn genuojn la tutan tempon.
Pamene zonsezi zinali kucitika, mwana mwamuna mung’ono wa Anansi anali imilile kuonelela pansi pacimtengo. Iye anati, “Kodi sicizakhala capafupi kukwela mtengo ngati mwamangilila mbiya kumusana?” Anansi anayesa kumangilila mbiya yodzala ndi nzelu kumusana ndipo iye anakwela mtengo mosabvutika.
La tutan tempon la juna filo de Anansi estis observanta malsupre ĉe la trunko de la arbo. Li diris, “Ĉu ne estus pli facile grimpi se vi anstataŭe ligus la kruĉon al via dorso?” Anansi provis ligi la argilan kruĉon plenan de saĝeco al sia dorso, kaj tio vere estis multe pli facila.
Posacedwa konse anafike pamwamba pa mtengo. Koma iye anaima naganiza, “Ine ndiyenela kukhala ndi nzelu zonse, koma apa mwana wanga ndiye anali ndi nzelu kupambanila ine!” Anansi anakalipa kwambili paizi motelo anataya mbiya ya nzelu pansi kucoka mucimtengo.
Tujtuje li atingis la supron de la arbo. Sed tiam li haltis pensante, “mi devus esti tiu kiu havas ĉiun saĝecon sed jen mia filo estis pli lerta ol mi!” Anansi estis tiel kolera pri tio ĉi ke li ĵetis la argilan kruĉon malsupren for de la arbo.
Mbiya inaphwanyika mtizidutswa itafika pansi. Pamenepo nzelu zinafalitsidwa kwa munthu aliyense. Ndiye mwamene anthu anaphunzilila kulima, kusoka zovala, kupanga zitsulo za nsimba ndi zinthu zina zimene anthu adziwa kucita.
Ĝi frakasiĝis en pecojn sur la tero. La saĝeco estis libera por dividiĝi inter ĉiuj. Kaj tiel la homoj lernis farmi, teksi tukojn, fari ferajn ilojn, kaj ĉiujn aliajn aferojn kiujn homoj scias fari.