Elŝuti PDF-on
Reiri al la rakontolisto

Kambewu: Nkhani ya Wangari Maathai La eta semo: la rakonto de Wangari Maathai

Verkita de Nicola Rijsdijk

Ilustrita de Maya Marshak

Tradukita de Gridon Mwale

Laŭtlegita de Christine Mwanza

Lingvo njanĝa

Nivelo 3-a nivelo

Laŭtlegi la tutan rakonton Sonregistraĵo por tiu ĉi rakonto ankoraŭ mankas.


Pamudzi wina womangidwa pamatero ya phiri la Kenya kumwawa kwa Africa, Kunali kamtsikana kena dzina lake Wangari. Wangari ndi amai ake anali kugwira ntchito zaminda.

En vilaĝo sur la deklivoj de la Monto Kenjo en Orienta Afriko, infanineto laboris en la kampoj kun sia patrino. Ŝia nomo estis Wangari.


Wangari anali mtsikana wokonda kucezera pabwalo. Tisku lina Wangari anagaula mudimba mwao nabzyala tumbewu pansi pomwe panali potentha kwambiri.

Wangari amis esti ekstere. En la manĝĝardeno de sia familio, ŝi disrompis la grundon per sia maĉeto. Ŝi premis semetojn en la varmetan teron.


Thawi imene anali kukonda kwambiri mtsikanayu tsiku lililonse inali pamene dzuwa litangolowa kumene. Ndipo mudima ukagwira chakuti zomera zamthengo zaleka kuoneka, Wangari anali kudziwa kuti thawi yopita ku nyumba yafika tsopano. Ndipo popita kunyumba anali kudzera njira zang’ombe, kuwoloka mitsinje ndi kudutsa minda mpaka kufika kwao.

Ŝia preferata horo de la tago estis tuj post la sunsubiro. Kiam la mallumo estis tro por vidi la plantojn, Wangari sciis ke venis la horo por hejmeniri. Ŝi sekvis the vojetojn tra la kampoj, trapasanta riverojn survoje.


Wangari anali mwana wocenjera kwambiri ndipo anali wofunitsitsa kupita kusukulu kukaphunzira. Koma makolo ake sanafune kuti kamtsikana aka kaphunzire koma kazikhala pa nyumba ndi kugwira ncthito. Pamene Wangari anali ndi zaka 7, mukulu wake wamwamuna anagonjetsa makolo awo pokambirana kuti Wangari apite kusukulu akaphunzire.

Wangari estis lerta infano kaj atendis senpacience studi lerneje. Sed ŝia patrino kaj patro volis ke ŝi restu hejmen por helpi ilin. Kiam ŝi estis sepjaraĝa, ŝia pli aĝa frato persvadis iliajn gepatrojn permesi ŝin eniri la lernejon.


Wangaari anakonda kuphunzira kwambir chotero kuti anaphunzira kopitirira kupyolera mkuwerenga mabuku osiyanasiyana. Ndipo anakhoza kwambiri pa sukulu chotero kuti anapeza umwayi wokaphunzira ku dziko lakutali la United States of America. Wangari anasangalala kwambiri chifukwa anali kufunitsitsa kudziwa zambiri zapa dziko lapansi.

Ŝi ŝatis lerni! Wangari lernis pli kaj pli de ĉiu libro legita. Ŝi faris tiom bone lerneje ke ŝi estis invitita studi en Usono. Wangari estis ekcitita! Ŝi volis scii pli pri la mondo.


Wangari anaphunzira zinthu zambiri pamene anali pa American Univeziti. Anaphunzira pa zomera ndi mumene zimakulira. Zimenezi zinamukumbutsa mumene anali kusewerera ndi abale ake mthunzi ya mitengo mthengo laku-dziko lokongola la Kenya.

En la Usona universitato Wanari lernis multajn novajn aferojn. Ŝi studis plantojn kaj kiel ili kreskas. Kaj ŝi memoris kiel ŝi kreskis: ludanta kun ŝiaj fratoj in la ombro de la arboj en la belaj Kenjaj arbaroj.


Pamene anali kuphunzira tsiku ndi tsiku anazindikira kuti akonda anthu akwao ku Kenya. Anali kufuna kuti anthu kudziko limeneli tsiku lina akapate ufulu ndi mtendere. Ndipo anayewa dziko lakwao pamene anapitiliza ndi maphunziro. ake kwakanthawi.

Ju pli ŝi lernis, des pli ŝi konstatis ke ŝi amis la homojn de Kenjo. Ŝi volis ke ili estu feliĉaj kaj liberaj. Ju pli ŝi lernis, des pli ŝi memoris sian Afrikan hejmon.


Anabwerera kudziko lakwao ku Kenya pamane anamaliza maphunziro ake ndipo nthawi imeneyi dziko la Kenya linali litasintha. Mapulazi akuluakulu anatenga malo ochuluka. Azimai anali kusowa kotheba nkhuni chifukwa mitengo kunalibe. Anthu anali osauka ndipo ana anali kuoneka anjala.

Kiam ŝi finis siajn studojn, ŝi revenis al Kenjo. Sed ŝia lando ŝanĝiĝis. Grandegaj bienoj etendis tra la lando. Hominoj ne havis lignon por fari kuirfajrojn. La homoj estis malriĉaj kaj la infanoj malsatis.


Wangari anali kudziwa chofunika kuchita kuti athetsa mabvuto amenewa: anaphunzitsa azimai kubzyala mitengo kuchokera kumbewu. Azimai amenewa anayamba kugulitsa mitengo zao zitakula ndikupeza ndalama zosamalira ma banja awo. Chifukwa cacimenechi azimai anakhala wokondwera kwambiri ndi Wangari amene anawa thandiza kuti akhale ndi mphanvu komanso olimba.

Wangari sciis kion fari. Ŝi instruis la hominojn kiel kreskigi arbojn de semoj. La inoj vendis la arbojn kaj uzis la monon por prizorgi siajn familiojn. La hominoj estis tre feliĉaj. Wangari helpis ilin senti potenca kaj forta.


Patapita zaka zambiri, mitengo zimene zinabzyalidwa zija, zinakula ndi ku panga thengo. Mitsinje inayambanso kukhala ndi madzi. Mbiri ya Wangari inafika ponseponse mu Africa. Lerolino, mitengo zamitundumitundu mamilyoni tilikuonazi zinachokera ku mbewu ya Wangari.

Dum tempo pasis, novaj arboj kreskis arbaren, kaj la riveroj reekfluis. La mesaĝo de Wangari disvastiĝis tra Afriko. Hodiaŭ, milionoj da arboj kreskis de la semoj de Wangari.


Wangari anasewenzadi mwamphanvu. Chotero kuti anthu dziko lonse lapnansi anazindikila ntchito yaikula yomwe anacita, ndipo ana patsidwa mphoto yodziwika kwambiri padziko lonse lapansi. Mphoto imeneyi inali kutchedwa kuti Kulemekezedwa ndi Mtendere, ndipo anakhala mkazi woyamba mu Africa kulandila mphoto yotero.

Wangari laboris diligente. Homoj ĉirkaŭ la mondo rimarkis, kaj donis al ŝi faman premion. Ĝi estas nomita la Pac-Premio de Nobel, kaj ŝi estis la unuan Afrikan hominon iam ricevi ĝin.


Wangari anamwalira mu caka ca 2011, koma timamukumbukila tikamaona mtengo wokongola uliwonse mthengo.

Wangari mortis en 2011, sed ni povas pensi pri ŝi ĉiufoje ke ni vidas belan arbon.


Verkita de: Nicola Rijsdijk
Ilustrita de: Maya Marshak
Tradukita de: Gridon Mwale
Laŭtlegita de: Christine Mwanza
Lingvo: njanĝa
Nivelo: 3-a nivelo
Fonto: A Tiny Seed: The Story of Wangari Maathai el la Afrika Rakontolibro
Krea Komunaĵo Permesilo
Ĉi tiu verko estas disponebla laŭ la permesilo Krea Komunaĵo Atribuite 4.0 Tutmonda.
Opcioj
Reiri al la rakontolisto Elŝuti PDF-on